VERSE ***1
Iwe satana.. pamalo pano
Choka choka iwe 2 Choka iwe Satana choka2
Thawi yatha iwe
Ndikufuna kupephela
Choka choka iwe
Choka iwe Satana choka***2
Pamalo pano podalisidwa
Choka choka iwe
Choka iwe Satana choka ***2
Chorus ***1
Koma undileke
Ndikufuna kulalika zayesu
Kulalika zayesu
Ndati undisiye chonde
Ndikufuna kuimbila zayesu
Kodi mvuto lako chiyani nanga
Ndikufuna kufalisa uthenga
Ndifalise uthenga
Wayesu khristu yekha
Ndikufuna kupembeza yehova
Kodi ulibe manyazi nanga?
Verse ***2
Usandiuze zaboza lako
Lakupha aii
Usandiuze zaboza lako
Lachigolo
Usandiuze za boza lako
Lakuba aiii
Usandiuze zaboza lako
Lachigololo
Chorus ***2
Athu ambiri akuzuzika
Chifukwa cha iwe
Unawapasa awa matenda
Osachidzika
Anawaphera ambale awo
Awa achikondi
Unanenela awa maboza
Lero amangidwa
Chorus ***3