Home » Lyrics » Praise Pemphero Kambela – Yesu Ndi Thanthwe Lyrics

Praise Pemphero Kambela – Yesu Ndi Thanthwe Lyrics

by Malawi Gospel Music
776 views
          *Verse 1* 

Mbuye ndi thanthwe lolimba, Ndipousira chimphepo,
M’zovuta takhazikika, ndi pousira chimphepo.
Ndiye mnthuzi pausana, Ndipousira chimphepo M’usiku saopsa mantha, Ndipousira chimphepo.

      *Chorus*

Yesu ndi thanthwe m’dziko lotopesa, lotopetsa, lotopetsa
Yesu ndi thanthwe m’dziko lotopetsa
Ndi pousira chimphepo.

     *Verse 2*

Namondwe akatizinga, Ndipousira chimphepo. Panopa sitisunthidwa, Ndipousira chimphepo,
Thanthwe langa looosira, Ndipousira chimphepo. Ndinu wotithangatira, Ndipousira chimphepo.

Chorus

Yesu ndi thanthwe m’dziko lotopesa, lotopetsa, lotopetsa
Yesu ndi thanthwe m’dziko lotopetsa
Ndi pousira chimphepo.

malawigospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel Music and any gospel News.malawigospelmusic.com offer services like song lyrics,Audio upload,poems,Music video upload on our You Tube channel called Malawian Gospel Music, Artist biography, Extended playlist (EP),Article, Album and Banner on website. For inquiry contact these numbers 0888 069 117/0885 572 836 or 0983 592 032/0994 56 15 46 or info@malawigospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media