Home » Lyrics » Praise Pemphero Kambela – Munyengo Zonse Lyrics

Praise Pemphero Kambela – Munyengo Zonse Lyrics

by Malawi Gospel Music
274 views
   *chorus*

Munyengozonsee,
Zonsee, inu ndinu Mulungu,x2
Simumasintha,
Munaliko muliyemweyo,
Kunthawizonse,
Simumasintha,
Mudzakhala m’paka mpakamuyaya.

Verse-(1)

Ndikudziwa, kulimapiri otindikweleee,!!
Ndikudziwa, kulimitsinje yoti ndiwolokee!!
Chomwe ndidziwa,
Simudzalola
phadzilanga litelelekeee!!
Chomwe ndidziwa,
Simudzalola,
Adanianga atsekeleee!!
Chomwe chilichanga,
Chidzakhalabe changaa!!
Palibe nyengo,
Yomwe idzabwele,
Yopotsa mtsikhuwangaa,!!
Nthawi imasintha,
Nyengo imasinthaaa!!
Dziko limasintha,
Koma Yehova ndinu wachikhalile.

Chorus

Munyengozonsee,
zonsee,
Inu ndinu Mulungu,x2
Simumasintha,
Munaliko muliyemweyo,
Kunthawizonse,
Simumasintha,
Mudzakhala m’paka
Muyaya.

   *Verse-(2)*

Abwenzi apadziko,
amakukonda Pamene
dzikuyendaa,
Koma zikathina!
onsewo amabalalikaa,!!
Nthawi imasintha,
Nyengo imasinthaa,
Dziko limasintha,
Koma Yehova,
Ndinu wachikhalile.x2

Chorus

Munyengozonsee,
Zonsee,
Inu ndinu Mulungu,x2
Simumasintha,
Munaliko muliyemweyo,
Kunthawizonse,
Simasintha mudzakhala,
M’paka Muyaya.

malawigospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel Music and any gospel News.malawigospelmusic.com offer services like song lyrics,Audio upload,poems,Music video upload on our You Tube channel called Malawian Gospel Music, Artist biography, Extended playlist (EP),Article, Album and Banner on website. For inquiry contact these numbers 0888 069 117/0885 572 836 or 0983 592 032/0994 56 15 46 or info@malawigospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media