Home » Lyrics » JUDITH SUWEDI FUNYA – LAPA M’BALE LYRICS

JUDITH SUWEDI FUNYA – LAPA M’BALE LYRICS

by Malawi Gospel Music
316 views

Vol 2.

Verse 1.

Dziko lino lapasi muli zinthu zambili,muli kusangalala komanso ndikulila komano kwayesuyo kulimoyo wosatha, ukalapa machimo udzalandila yesu,nthawi musewelesai ena mmatembelelo,nthawi musewelesai kwaena akudalitsika,nthawi musewelesai ena akumwalila nthawi yokhayokhayo ena akulapa tchimooo

Chorus

Iwe lapa m baleee
nthawi yako isanathe
Siya tchimo
nthawi Yako ndiyomwei
Iwe lapa m bale
nthawi Yako isanathe
Lapalapa
nthawi Yako ndiyomwei
Iwe lapa m bale!!
nthawi yako isanathe
Siya tchimo
nthawi Yako ndiyomwei
Iwe lapa m bale
nthawi Yako isanathe
Siya bodza
nthawi Yako ndiyomwei
Iwe lapa m bale,Siya kuba
nthawi Yako isanathe
Iwe lapa m bale lapalapa
nthawi Yako ndiyomwei

Verse 2.

Nthawi ino abale siyochedwa ndi tchimo,nthawi ino abale ndiyolandila yesu ,nthawi ino anabe siyongodandaula,nthawi yokhayokhayo ena alandile yesu,tikamakhala abale tidziwe kuli mulungu konse kumene tiyenda ngakhale pa babja pathu,tikamachita machimo tiziwe mbuye amaona,Mulungu ndiye mzimu amaona ponsepoooo

Verse 3.

Dziko lino lapasi muli zinthu zambili muli kusangalala komaso ndikulila komano kwayesuyo kuli moyo wosatha,ukalapa machimo udzalandila yesu,nthawi musewelesai ena mmatembelelo,nthawi musewelesai kwa ena akudalisika,nthawi musewelesai ena akumwalila,nthawi yokhayokhayo ena akulapa tchimoo

malawigospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel Music and any gospel News.malawigospelmusic.com offer services like song lyrics,Audio upload,poems,Music video upload on our You Tube channel called Malawian Gospel Music, Artist biography, Extended playlist (EP),Article, Album and Banner on website. For inquiry contact these numbers 0888 069 117/0885 572 836 or 0983 592 032/0994 56 15 46 or info@malawigospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media