Home » Lyrics » ISRAEL – YESU BWENZI LYRICS

ISRAEL – YESU BWENZI LYRICS

by Malawi Gospel Music
350 views

(Hook)

Ooh Yesu wanga
(Ndibwenzi)
Ooh Yesu Wanga
(Eeeh ndibwenzi)
Ooh Yesu wanga
(Ndibwenzi)
Ndibwenzi Lokometsetsa..
Ooh Yesu wanga
(Ndibwenzi)
Ooh Yesu Wanga
(Eeeh ndibwenzi)
Ooh Yesu wanga
(Ndibwenzi)
Ndibwenzi lokondetsetsa..

(Verse)

Abwenzi Am’dziko timakhala nawo//
Kwanthawi yochepa ndikusiyana//
Dzuwa likalowa titsanzikana//
Mugone bwino tionana mawa//
Tikasiyana palibe amadziwa//
Chimene chimchitikila nzakeyo//
Pokhapokha alandile uthenga//
Nzako wadwala ‘pena wamwalira//
Koma ndili ndibwenzi langa lokonda//
Nthawi zonse samandisiya//
Kulikonse kumene ndingapite//
Akhala nane kundiyang’anira//
Samagona kapena kuodzera//
Amanditeteza usiku onse//
M’banda kucha andidzutsa ndimphamvu//
Masana, madzuro akhala nane//

malawigospelmusic.com is a Christian music website with all Malawian gospel Music and any gospel News.malawigospelmusic.com offer services like song lyrics,Audio upload,poems,Music video upload on our You Tube channel called Malawian Gospel Music, Artist biography, Extended playlist (EP),Article, Album and Banner on website. For inquiry contact these numbers 0888 069 117/0885 572 836 or 0983 592 032/0994 56 15 46 or info@malawigospelmusic.com

All Rights Reserved – Designed and Developed by Kay Dee Media